Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Sports Sports

Queens yafa ndi South Africa

Queens yagonja 65-35 ndi South Africa mu mpikisano wa m’mayiko a mu Africa umene ukuchitikira m’dziko la Namibia.

Malawi, yomwe inagonjetsa Zambia mu masewero ake oyamba, inatsalira m’zigawo zonse zinayi za masewerowo.

Apa ndiye kuti timuyi ili pa nambala yachiwiri mu Gulu A momwe mulinso ma timu a Kenya ndi Zambia.

Ma timu awiri omwe amalize pamwamba pa gululi apitilira mu ndime ya semifainolo.

Timuyi isewera masewero ake omaliza a m’magulu lachinayi lino pomwe ikumane ndi timu ya Kenya.

Olemba: Amin Mussa

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Ayamikira Chitukuko cha milatho

MBC Online

President Chakwera to preside over SACAU’s opening session in Lilongwe

Romeo Umali

Lero ndi tsiku lokumbukira matenda a Fistula

Lonjezo Msodoka
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.