Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

President Chakwera akhala nawo pamwambo wa mapemphero

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akhala nawo pa mwambo wa mapemphero pa mpingo wa Monkey Bay Assemblies of God m’boma la Mangochi.

Mwambo wa mapemphero umenewu ukuyembekezeka kuyamba nthawi ya 9 koloko m’mawa uno.

President Chakwera ali m’chigawo chaku m’mawa kumene akugwira ntchito zaboma.

Olemba: Owen Mavula

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Govt committed to reducing road accidents – Daud

MBC Online

Sanwecka honours pledge to EOY winners

MBC Online

POLICE RESCUE TWO FROM MOB

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.