Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Nyakwawa ikakhala ku ndende pamlandu wogwililira

Khoti la Magistrate ku Phalombe lalamula nyakwawa Nayuma, yomwe dzina lake ndi Leonard Julius, kukakhala kundende zaka 12 chifukwa chogwililira mtsikana wazaka 14.

Mneneri wapolisi ku Phalombe, Jimmy Kapanja, wati izi zinadziwika mwezi wa October chaka chatha.

Malinga ndi a Kapanja, pakadali pano mtsikanayo, yemwe amadwala matenda a mu ubongo, ali ndi mwana wa nyakwawayo.

 

Related posts

Karonga Diocese denounces violence on older persons, children

MBC Online

ENERGY PUMPS IN K19 MILLION TOWARDS EDUCATION FOR THE UNDERPRIVILEGED

Romeo Umali

Good Neigbours donate medical drugs to LL DHO

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.