Malawi Broadcasting Corporation
Development Education Local Local News Nkhani

Madam Chakwera atsegula sukulu ya Chiyola CDSS

Mayi wa pfuko lino, Madam Monica Chakwera, atsegulira sukulu yatsopano ya sekondale yoyendera ya mdera la Chiyola m’boma Rumphi imene bungwe la Press Trust lamanga.

Sukuluyi ili ndi zipinda zofunika monga makalasi ophunzirira ngakhalenso chipinda chosungira mabuku.

Themba la Mathemba Chikulamayembe athokoza boma popititsa patsogolo maphunziro m’dziko muno ndipo ati chiyembekezo kuti derali litukuka kwambiri m’magawo osiyanasiyana chifukwa cha sukuluyi.

Iwo atinso atsikana mderali amayenda mtunda wautali kuti akapeze maphunziro ku sukulu za Mwasizi ngakhalenso Katowo.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Mayi amangidwa poganiziridwa kuti wapha mwamuna wake

Romeo Umali

Ecobank launches new internet banking feature

Arthur Chokhotho

Ifenso tikuthandiza pa ntchito zokopa alendo —Daza

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.