Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Kambwiri ayikidwa mmanda mawa

Thupi la amene anali mkhalakale pa nkhani zoulutsa mawu, Joshua Kambwiri, alitengera ku mudzi kwawo ku Domasi m’boma la Zomba, kumene akaliyike m’manda mawa Lolemba.

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi malemu Kambwiri unachitikira pa tchalitchi cha Ngumbe CCAP ku Chileka munzinda wa Blantyre kumene malemuwa amapemphera.

Malemu Kambwiri, amene anagwirapo ntchito ku nyumba youlutsa mawu ya MBC, amwalira ali ndi zaka 62.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Government to unveil K7BN grant for MSEs

MBC Online

Dedza MET worried over vandalism

Sothini Ndazi

MALAWI BROADCASTING CORPORATION EXECUTIVE MANAGEMENT PLACEMENT: DIRECTOR OF HUMAN RESOURCE AND ADMINISTRATION

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.