Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

Kambwiri ayikidwa mmanda mawa

Thupi la amene anali mkhalakale pa nkhani zoulutsa mawu, Joshua Kambwiri, alitengera ku mudzi kwawo ku Domasi m’boma la Zomba, kumene akaliyike m’manda mawa Lolemba.

Mwambo wa mapemphero otsanzikana ndi malemu Kambwiri unachitikira pa tchalitchi cha Ngumbe CCAP ku Chileka munzinda wa Blantyre kumene malemuwa amapemphera.

Malemu Kambwiri, amene anagwirapo ntchito ku nyumba youlutsa mawu ya MBC, amwalira ali ndi zaka 62.

Related posts

Rumphi District Council constructs new IFMIS office

Rabson Kondowe

Chipatala cha Mponela chitha mwezi wa June 2025

Yamikani Simtowe

Tiwapatsa mwayi wa ngongole kuti apeze mpamba — TEVETA

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.