Malawi Broadcasting Corporation
Education Local Local News Nkhani

Emmanuel University idziphunzitsa Kiswahili

Sukulu ya ukachenjede ya Emmanuel imene ndi ya mu mnzinda wa Lilongwe yalengeza zoyamba kuphunzitsa Kiswahili ngati phunziro lapadera.

Izi zadziwika pa mwambo okondwelera chilankhulochi kumene kuli kazembe wa dziko lino mayi Agnes Kayola amene akuyembekeza mtsogoleri wa dziko la Tanzania mayi Samia Suluhu Hassan kuti achite zoyankhula kudzera pa uthenga wa pa kanema.

Pa malo amene pakuchitikira mwambowu pakuyankhulidwa ziyankhulo za Kiswahili, Chichewa ndi Chingerezi.

 

Related posts

Boma lati alimi atha kukolora zochuluka

Romeo Umali

Chakwera calls for renewed commitment

Alinafe Mlamba

Veep calls for immediate Forest Policy reforms

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.