Malawi Broadcasting Corporation
Education Local Local News Nkhani

Emmanuel University idziphunzitsa Kiswahili

Sukulu ya ukachenjede ya Emmanuel imene ndi ya mu mnzinda wa Lilongwe yalengeza zoyamba kuphunzitsa Kiswahili ngati phunziro lapadera.

Izi zadziwika pa mwambo okondwelera chilankhulochi kumene kuli kazembe wa dziko lino mayi Agnes Kayola amene akuyembekeza mtsogoleri wa dziko la Tanzania mayi Samia Suluhu Hassan kuti achite zoyankhula kudzera pa uthenga wa pa kanema.

Pa malo amene pakuchitikira mwambowu pakuyankhulidwa ziyankhulo za Kiswahili, Chichewa ndi Chingerezi.

 

Related posts

‘Ku Ntchisi kuli luso lamasewero’

Romeo Umali

Chakwera wants ministers to deliver — Commentators

MBC Online

Boma lakhazikitsa ntchito yogawa ufa kwa mabanja omwe akhudzidwa ndi njala

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.