Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Dr Chakwera apereka K5 million zothandizira pamaliro a Kasambara

Mtsogoleri wa dziko lino Dr Lazarus Chakwera wapereka ndalama zokwana K5 million kuti zithandizire pamwambo wa maliro a Raphael Kasambara omwe atisiya masiku apitawa.

A Harry Mkandawire, amene akuyimira Dr Chakwera, ati malemu a Raphael Kasambara anali munthu okonda kumenyera ufulu wa anthu osauka.

Iwo ati boma lisowa ntchito zambiri zomwe malemuwa anathandizirapo maaka pa chitukuko.

A Mkandawrire ayankhula izi pamene mwambo wa maliro uli mkati m’boma la Nkhata Bay.

Related posts

Akakhala kundende zaka 14 chifukwa chogwilira wamisala

Romeo Umali

Masewero a lero ndi masamu — Kayira

Romeo Umali

Boma ligula PREP ochuluka chaka chamawa

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.