Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Religion

Dr Chakwera akumana ndi atsogoleri azipembedzo

Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno akuyembekezeka kukumana ndi atsogoleri azipembedzo zosiyanasiyana ku nyumba ya boma ya Chikoko Bay m’boma la Mangochi.

Pakadali pano, atsogoleri oyimira zipembedzo ayamba kufika ku zokambilanazi.

Dr Chakwera ali m’chigawo cha kummawa kumene akugwira ntchito zosiyanasiyana za boma.

Olemba: Owen Mavula

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Castel Malawi awards long-serving employees

Yamikani Simutowe

Two die after taking alcohol on empty stomach

Jeffrey Chinawa

MALAWI HAS POTENTIAL IN AI —TECH EXPERT

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.