Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Religion

Dr Chakwera akumana ndi atsogoleri azipembedzo

Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno akuyembekezeka kukumana ndi atsogoleri azipembedzo zosiyanasiyana ku nyumba ya boma ya Chikoko Bay m’boma la Mangochi.

Pakadali pano, atsogoleri oyimira zipembedzo ayamba kufika ku zokambilanazi.

Dr Chakwera ali m’chigawo cha kummawa kumene akugwira ntchito zosiyanasiyana za boma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

17 years for sleeping with a minor

Romeo Umali

SPEAKER SUSPENDS HOUSE BRIEFLY

MBC Online

First Lady calls for collaboration in supporting needy students

Secret Segula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.