Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Religion

Dr Chakwera akumana ndi atsogoleri azipembedzo

Mtsogoleri wadziko lino Dr Lazarus Chakwera m’mawa uno akuyembekezeka kukumana ndi atsogoleri azipembedzo zosiyanasiyana ku nyumba ya boma ya Chikoko Bay m’boma la Mangochi.

Pakadali pano, atsogoleri oyimira zipembedzo ayamba kufika ku zokambilanazi.

Dr Chakwera ali m’chigawo cha kummawa kumene akugwira ntchito zosiyanasiyana za boma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

GAS DISTRIBUTORS URGED TO BROADEN SALES

MBC Online

Munthu mmodzi wavulala modetsa nkhawa pa ngozi ya sitima

Romeo Umali

Blantyre District Netball Committee secures player of the week sponsorship

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.