Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

President Chakwera akhala nawo pamwambo wa mapemphero

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, lero akhala nawo pa mwambo wa mapemphero pa mpingo wa Monkey Bay Assemblies of God m’boma la Mangochi.

Mwambo wa mapemphero umenewu ukuyembekezeka kuyamba nthawi ya 9 koloko m’mawa uno.

President Chakwera ali m’chigawo chaku m’mawa kumene akugwira ntchito zaboma.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Malawi International Arbitration Centre gets financial boost

Rabson Kondowe

Creck hold Bullets in 2025 Airtel Top 8 opener

Romeo Umali

People gather at Mangunda for Major Selemani’s funeral

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.