Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

A Nankhumwa akhazikitsa chipani

Mtsogoleri wa chipani chatsopano cha People’s Development (PDP), Kondwani Nankhumwa, wati chipanichi chabwera kudzasintha Malawi kukhala dziko lodzidalira pa chakudya, la umodzi ndinso kulimbikira pantchito.

Poyankhula pamsonkhano wa atolankhani mumzinda wa Blantyre, iwo ati chipanichi chithetsa m’chitidwe okakamira m’maudindo muzipani.

A Nankhumwa atinso a Malawi akufunika chipani chomwe chingamalore anthu kupikisana momasuka.

Wolemba: Blessings Cheleuka

Related posts

Osakhala, kuchita malonda pafupi ndi njanji — Boma

Yamikani Simtowe

A Chakwera ali mu mzinda wa Mzuzu

Alinafe Mlamba

Msewu wa Nkhotakota tiumaliza komanso ukhala wapamwamba – Chakwera

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.