Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi alanda makina opangira ndalama zachinyengo

Apolisi ku Chileka mu mzinda wa Blantyre amanga anthu anayi atapezeka ndi ndalama zachinyengo zokwana K915,000.

M’neneri wa polisi ya Chileka, a Jonathan Phillipo, wati apolisiwo akwanitsanso kulanda makina amene anthuwo amagwiritsa ntchito popanga ndalama zachinyengozo.

 

Related posts

Transformative Leadership Programme, a Game Changer

Alinafe Mlamba

Pastor Eneche jets in Malawi

Romeo Umali

Karonga United triumph over Baka City

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.