Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local Local News

ADMARC ayipatsa K 40 Billion yogulira chimanga

Bungwe la Admarc lapatsidwa ndalama zokwana K40 billion kuti liyambenso kugwira ntchito zake modalirika komanso kuyamba kuyendetsa ntchito zake ngati bungwe lochita malonda.

Nduna ya zachuma, a Simplex Chithyola Banda, anena izi pamene akupereka ndondomeko yazachuma ya chaka chaboma cha 2024/2025.

A Banda ati National Food Reserve Agency yapatsidwa K12 billion yogulira chimanga.

Related posts

Dedza DEST urged to be professional ahead of 2025 polls

Rabson Kondowe

32 percent of Malawians die from NCD

Secret Segula

Zaka zitatu pogulitsa makala mosatsata lamulo

Mayeso Chikhadzula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.