Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local Local News

ADMARC ayipatsa K 40 Billion yogulira chimanga

Bungwe la Admarc lapatsidwa ndalama zokwana K40 billion kuti liyambenso kugwira ntchito zake modalirika komanso kuyamba kuyendetsa ntchito zake ngati bungwe lochita malonda.

Nduna ya zachuma, a Simplex Chithyola Banda, anena izi pamene akupereka ndondomeko yazachuma ya chaka chaboma cha 2024/2025.

A Banda ati National Food Reserve Agency yapatsidwa K12 billion yogulira chimanga.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Aphwanya malamulo la chipani cha UTM— Kondowe

MBC Online

CHAKWERA LAUNCHES 2022 AIP

MBC Online

MW, ICELAND IN BILATERAL TALKS 

Blessings Kanache
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.