Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Development Local Local News

ADMARC ayipatsa K 40 Billion yogulira chimanga

Bungwe la Admarc lapatsidwa ndalama zokwana K40 billion kuti liyambenso kugwira ntchito zake modalirika komanso kuyamba kuyendetsa ntchito zake ngati bungwe lochita malonda.

Nduna ya zachuma, a Simplex Chithyola Banda, anena izi pamene akupereka ndondomeko yazachuma ya chaka chaboma cha 2024/2025.

A Banda ati National Food Reserve Agency yapatsidwa K12 billion yogulira chimanga.

Related posts

Kamberembere wobera anthu kudzera pa masamba a mchezo amumanga

Romeo Umali

Artists unite to address issues affecting their welfare

Romeo Umali

Women’s Manifesto launched with a call for action.

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.