Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Mwezi sunaoneke, tchuthi lachinayi —MAM

Bungwe la asilamu la Muslim Association of Malawi (MAM) lati mwezi otsiriza kusala kudya wa Ramadan sunaoneke, choncho iwo ati Eid idzakhalapo lachinayi.

Mneneri wa bungweli, Sheikh Dinala Chabulika, auza MBC kuti zateremu ndiye kuti asilamu atsiriza kusala kudya mawa lachitatu ndipo tchuthi cha Eid chidzachitika lachinayi likudzali.

Related posts

Chakwera arrives in Rome

Alinafe Mlamba

System launched

McDonald Chiwayula

ASSOCIATION OF MEDICAL COUNCILS OF AFRICA ANNUAL CAPACITY-BUILDING WORKSHOP JOINTLY HOSTED BY THE MEDICAL COUNCIL OF MALAWI AND THE MINISTRY OF HEALTH

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.