Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Mwezi sunaoneke, tchuthi lachinayi —MAM

Bungwe la asilamu la Muslim Association of Malawi (MAM) lati mwezi otsiriza kusala kudya wa Ramadan sunaoneke, choncho iwo ati Eid idzakhalapo lachinayi.

Mneneri wa bungweli, Sheikh Dinala Chabulika, auza MBC kuti zateremu ndiye kuti asilamu atsiriza kusala kudya mawa lachitatu ndipo tchuthi cha Eid chidzachitika lachinayi likudzali.

Related posts

Activists want sanitary pads accessible for free

Alinafe Mlamba

NYIKA MEDIA CLUB PLEDGES TO HYPE HOSPITALITY INDUSTRY

MBC Online

Opindula ndi Mtukula Pakhomo alandira dipo lawo pa lamya

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.