Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Sports Sports

Wanderers yavomereza Mwase

Meke Mwase amusakha ngati mphunzitsi watimu ya Mighty Mukuru Wanderers kulowa m’malo mwa Nsazurwimo Ramadan yemwe anatula pansi udindowu mwezi wa May.

A Ramadan anatula pansi udindo ngati mphunzitsi kutsatira kusachita bwino kwa timuyi.

Mwase wakhala ali mphunzitsi ogwilizira ku timuyi.

Iye akusankhidwa pamene timuyi ili panambala yachiwiri mu super ligi ndi mapointi 41.

Olemba: Praise Majawa

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Govt optimistic about reviving international agro-business deals

Earlene Chimoyo

Tisewera kuti tibwezeretse ulemu wathu – Mabedi

Paul Mlowoka

Matupi ena angozi ya ndege awaika m’manda masanawa

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.