Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Ndi mlandu kugulitsa, kuononga ndalama zachitsulo — Banki ya Reserve

Banki yayikulu m’dziko muno ya Reserve yati lamulo ligwira ntchito kwa anthu onse amene akugulitsa, kugula ndi kuononga ndalama za chitsulo.

Mu chikalata chomwe wasayinira ndi Gavanala wa bankiyi, a Wilson Banda, bankiyi yati olakwa adzilipira chindapusa chokwana K5 million.

M’sabata zapitazi, anthu ambiri akhala akutsatsa ndalama zachitsulo monga K5 ndi K10 ndipo zadziwika kuti anthuwa amasungunula ndi kuphwanya ndalamazi.

 

Related posts

LL District Council completes 50 key infrastructure projects in 3 Years

Alinafe Mlamba

Parliament amends bill to revise investment into Salima – Lilongwe Water project

Romeo Umali

Education ministry eyes ODeL expansion as learner numbers rise

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.