Malawi Broadcasting Corporation
Nkhani

Mwana wamwalira makolo ake atakana kumutengera kuchipatala

Apolisi ku Zomba amanga Frederick Masiku wazaka 46 ndi mkazi wake Fasilen Golosi wazaka 38 chifukwa chokaniza kutengera mwana wawo kuchipatala chifukwa cha chipembedzo.

Mneneri wapolisi ku Zomba Patricia Sipiliano wati mwana wa banjalo wazaka zisanu anadwala mutu. Kenako banjalo linayamba kupemphelera mwanayo koma mwatsoka anamwalira.

Banjali ndi la mmudzi wa Ramusi 2 Mfumu yaikulu Ramusi ku Zomba.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

MCP yadzipereka kukweza chigwa cha Shire

MBC Online

Talandira K6 miliyoni koma siyokwanira — Silver Strikers

Emmanuel Chikonso

Boma limanga sukulu zamkombaphala zokwana 150

Davie Umar
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.