Malawi Broadcasting Corporation
Environment Local Local News Nkhani

MVULA YABWERANSO

Nthambi yowona za nyengo m’dziko muno yati mvula ikhala ikugwa mpakana sabata ya mawa, pamene yayamba kuvumba m’maboma ambiri kuyambira loweruka m’mawa.

Ena ati zimenezi zitha kupangitsa kuti mbewu zosiyanasiyana, zimene zinayamba kunyala chifukwa cha ng’amba, zitsitsimuke pamene mvula yagwa.

Kubwera kwa mvulaku kwaika chikhulupiliro mea ambiri kuti mwina alimi akhoza kukolora mokwanira, zimene zingathandize kupewa njala.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Dr Chakwera apereka K5 million zothandizira pamaliro a Kasambara

Chisomo Manda

UN commits support to 2025 electoral process

MBC Online

Ng’oma mourned

Olive Phiri
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.