Malawi Broadcasting Corporation
Environment Local Local News Nkhani

MVULA YABWERANSO

Nthambi yowona za nyengo m’dziko muno yati mvula ikhala ikugwa mpakana sabata ya mawa, pamene yayamba kuvumba m’maboma ambiri kuyambira loweruka m’mawa.

Ena ati zimenezi zitha kupangitsa kuti mbewu zosiyanasiyana, zimene zinayamba kunyala chifukwa cha ng’amba, zitsitsimuke pamene mvula yagwa.

Kubwera kwa mvulaku kwaika chikhulupiliro mea ambiri kuti mwina alimi akhoza kukolora mokwanira, zimene zingathandize kupewa njala.

Related posts

Malawi envoy optimistic about China-Africa summit

Rabson Kondowe

Waste management: a solution to Covid-19 impact – Waste Advisers

Romeo Umali

Sports analyst urges Malawi Beach Soccer to utilise home ground

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.