Malawi Broadcasting Corporation
Development Local News Nkhani

Musapereke za unzika kwa aliyense — Kunkuyu

Boma ladzudzula m’chitidwe omwe anthu ena akumachita otenga ziphaso za unzika za anthu ena powanamiza kuti awamangira nyumba, mwa zina.

Nduna yofalitsa nkhani, a Moses Kunkuyu, atsindikiza izi lero mu mzinda wa Blantyre komwe anati boma likhazikitsa zilango zokhwima zomwe zidzagwire ntchito kwa aliyense opezeka olakwa.

Iwo ati m’chitidwewu ndi osavomerezeka ndipo aMalawi akhale tcheru ndikukaneneza ku Polisi onse amene akuchita izi.

Olemba: Timothy Kateta

Related posts

Bungwe lathandiza maanja 20,000 kuthana ndi njala

Alinafe Mlamba

A Mnjale amwalira

Mayeso Chikhadzula

Mining Minister seeks expert assistance

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.