Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Msika wa fodya wayamba bwino ku Limbe

Alimi a fodya m’dziko muno ati ndiosangalala ndi m’mene malonda a fodya ayambira pa msika.

President wa Tobacco Association of Malawi (TAMA) trust, a Abiel Kalima Banda, ati mitengo ya fodya ya chaka chino yaposa zaka zam’mbuyomu.

“Mitengo imeneyi ilimbikitsa alimi pa ulimi wawo,” atero a Kalima Banda.

Malonda a fodya ku Limbe ayamba pa mtengo wa  3 dollars 11 cents ndipo mtengo otsika ndi 2 dollars 20 cents.

Related posts

China supports KCH with medical equipment

Romeo Umali

Community ART groups curb ARV default among youth in Chiradzulu

Rabson Kondowe

Disability inclusion concerns raised at National Tally Centre

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.