Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local News Nkhani

Mikozi ibweranso, eni ake atero

Mwini watsamba la mchezo la Mikozi, a Bright ‘Excess’ Chiligo, watsutsa mphekesera zimene zikumveka kuti tsamba lake anthu alichita chiwembu kuti lisowe pa makina a internet.

Chiligo wati tsambali libweleranso Lachisanu chifukwa pali ntchito imene akugwira yopanga tsambali kukhala lotetezeka kwa anthu achinyengo.

“Tawona kuti pa internet pachuluka masamba a mchezo amene akubera dzina lathu la Mikozi ndipo akumayika zinthu zoyipa,” iye anatero.

Anawonjezeranso kuti zimenezi zapangitsa kuti azilandira madandaulo ochuluka kuchokera kwa anthu.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Chakwera launches 2024 Poppy Appeal Week

Beatrice Mwape

NICE advocates for inclusive participation in voter registration

MBC Online

YONECO trains journalists to enhance reporting on albinism rights

Arthur Chokhotho
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.