Malawi Broadcasting Corporation
Development Local News

Matupi ena angozi ya ndege awaika m’manda masanawa

Matupi ena a abale asanu ndi m’modzi (6) amene adatisiya pa ngozi ya ndege ku Chikangawa m’boma la Mzimba, anyamuka kupita ku maboma osiyanasiyana kuti akaikidwe n’manda.

Ma pulogalamu akuti a Lucas Kapheni ndi a Chisomo Chimaneni omwe amagwira ntchito ku Polisi akawaika lero ku Kasungu ndi ku Ntchisi ndipo ena akaikidwa mawa pa 14 June.

Ena akulowera ku Thyolo kumene kukayikidwe Major Flora Selemani Ngwinjili ndipo Colonel Owen Sambalopa akayikidwa ku Zomba ndipo Major Wales Aidini akayikidwa ku Mangochi pamene Daniel Kanyemba ayikidwa ku Lilongwe.

By Mirriam Kaliza
#MBCDigital
#Manthu

Related posts

Malawi makes progress in HIV/AIDS fight

Romeo Umali

Govt, UNDP launch Africa Green Business and Financing Initiative Roadmap

Alinafe Mlamba

Politics will not disturb Parliament — Suleman

Yamikani Simtowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.