Malawi Broadcasting Corporation
Development Local News

Matupi ena angozi ya ndege awaika m’manda masanawa

Matupi ena a abale asanu ndi m’modzi (6) amene adatisiya pa ngozi ya ndege ku Chikangawa m’boma la Mzimba, anyamuka kupita ku maboma osiyanasiyana kuti akaikidwe n’manda.

Ma pulogalamu akuti a Lucas Kapheni ndi a Chisomo Chimaneni omwe amagwira ntchito ku Polisi akawaika lero ku Kasungu ndi ku Ntchisi ndipo ena akaikidwa mawa pa 14 June.

Ena akulowera ku Thyolo kumene kukayikidwe Major Flora Selemani Ngwinjili ndipo Colonel Owen Sambalopa akayikidwa ku Zomba ndipo Major Wales Aidini akayikidwa ku Mangochi pamene Daniel Kanyemba ayikidwa ku Lilongwe.

By Mirriam Kaliza
#MBCDigital
#Manthu

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Tabitha wakankha chikopa mogometsa mu February ku France

Emmanuel Chikonso

MCP DIASPORA NETWORK READY TO SUPPORT MEGA FARMS INITIATIVE

MBC Online

Unofficial results puts independent candidate Phiri in the lead

Secret Segula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.