Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Kampani zamigodi ziyike umwini pa MSE — Misalico

Bungwe la Minority Shareholders Association of Listed Companies (Misalico) lati boma liwonetsetse kuti kampani za migodi zidziyika umwini wake wina pa msika wa Malawi Stock Exchange (MSE) kuti a Malawi adzigula nawo magawo.

Mlembi wa bungweli, a Frank Harawa, amafotokoza izi pamene msonkhano wa zamigodi watha lero mu mzinda wa Lilongwe.

Bungwe la Misalico ndi la anthu amene ali ndi masheya pa msika wa Malawi Stock Exchange.

Mukanema ali m’munsiyu, a Harawa akufotokoza zambiri.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Tax measures

Earlene Chimoyo

Malawians urged to protect biodiversity

MBC Online

MCP yayamikira anthu aku Mangochi powakhulupilira

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.