Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Dr Chakwera wabwelera ku Lilongwe

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wanyamuka ku Blantyre kubwelera ku Lilongwe atatsekulira chionetsero chazamalonda ku Chichiri Trade Fair grounds.

Wapampando wa chipani cha MCP m’chigawo chakummwera, a Peter Simbi, akuluakulu ena aboma komanso atsogoleri andale ndi mafumu ndi ena mwa omwe anapelekeza Dr Chakwera komanso First Lady Madam Monica Chakwera pabwalo la ndege la Chileka.

Olemba: Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

BULLETS SEAL K975 MN SPONSORSHIP DEAL

MBC Online

We are on towards achieving Malawi 2063 – Chakwera

MBC Online

SDA CHURCHES  HOLD REVIVAL WEEK AHEAD OF  CENTENARY CELEBRATIONS

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.