Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Dr Chakwera wabwelera ku Lilongwe

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wanyamuka ku Blantyre kubwelera ku Lilongwe atatsekulira chionetsero chazamalonda ku Chichiri Trade Fair grounds.

Wapampando wa chipani cha MCP m’chigawo chakummwera, a Peter Simbi, akuluakulu ena aboma komanso atsogoleri andale ndi mafumu ndi ena mwa omwe anapelekeza Dr Chakwera komanso First Lady Madam Monica Chakwera pabwalo la ndege la Chileka.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

Government says vocational training crucial as 750 graduate

Steve Dakalira

Water springs new hope at Thekerani Health Centre

Steve Dakalira

Irrigation key to food security, farmers appeal for assistance

Steve Dakalira
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.