Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Dr Chakwera wabwelera ku Lilongwe

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wanyamuka ku Blantyre kubwelera ku Lilongwe atatsekulira chionetsero chazamalonda ku Chichiri Trade Fair grounds.

Wapampando wa chipani cha MCP m’chigawo chakummwera, a Peter Simbi, akuluakulu ena aboma komanso atsogoleri andale ndi mafumu ndi ena mwa omwe anapelekeza Dr Chakwera komanso First Lady Madam Monica Chakwera pabwalo la ndege la Chileka.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

OVER 400 LEARNERS TO BENEFIT FROM STEPHANOS FOUNDATION ECD CENTRE

MBC Online

AFTER CYCLONE FREDDY, HOW TO STRENGTHEN MALAWI’S DISASTER PREPAREDNESS?

MBC Online

MW, PARTNERS LAUNCH MULTI-DONOR TRUST FUND

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.