Malawi Broadcasting Corporation
Uncategorized

Dr Chakwera wabwelera ku Lilongwe

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, wanyamuka ku Blantyre kubwelera ku Lilongwe atatsekulira chionetsero chazamalonda ku Chichiri Trade Fair grounds.

Wapampando wa chipani cha MCP m’chigawo chakummwera, a Peter Simbi, akuluakulu ena aboma komanso atsogoleri andale ndi mafumu ndi ena mwa omwe anapelekeza Dr Chakwera komanso First Lady Madam Monica Chakwera pabwalo la ndege la Chileka.

Olemba: Blessings Cheleuka

Related posts

CHAKWERA IMPRESSED WITH NKHATA-BAY WATER PROJECT PROGRESS

McDonald Chiwayula

Voters urged to verify names ahead of By-Elections

Steve Dakalira

Malawi among countries charting new civic spaces for Southern Africa

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.