Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Anthu akukhamukira kumwambo wa Chikumbutso ku Mulanje

Khwimbi la anthu likukhamukira ku bwalo la zamasewero la Mulanje kumene kukhale mwambo wokumbukira kuti patha chaka chimodzi chichitikireni Namondwe wa Freddy.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, ndiye atsogolere nwambowu komwe kwafika kale anthu osiyanasiyana, kuphatikizapo mafumundi akuluakulu ena.

Olemba : Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

‘Malo nawa koma tionepo chitukuko pasanathe zaka ziwiri’

Paul Mlowoka

Corruption over relief items worries President Chakwera, Paramount Chief Kyungu

MBC Online

MINDSET CHANGE CRUCIAL IN DEMYSTIFYING INFERTILITY – FIRST LADY

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.