Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Anthu akukhamukira kumwambo wa Chikumbutso ku Mulanje

Khwimbi la anthu likukhamukira ku bwalo la zamasewero la Mulanje kumene kukhale mwambo wokumbukira kuti patha chaka chimodzi chichitikireni Namondwe wa Freddy.

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, ndiye atsogolere nwambowu komwe kwafika kale anthu osiyanasiyana, kuphatikizapo mafumundi akuluakulu ena.

Olemba : Blessings Cheleuka

Related posts

Self-help initiatives springing up in Mwanza

Alinafe Mlamba

KAONGA ELECTED PRESIDENT OF PRISAM SACCO

McDonald Chiwayula

World Bank appoints Firas Raad as Malawi’s Country Manager

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.