Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Ali m’chitokosi pogonana ndi mwana

A Polisi m’boma la Chiradzulu anjata a John Mapoko a zaka 30 omwe ndi m’phunzitsi pa sukulu ya pulaimale ya Mulirankhwali kaamba kowaganizira kuti anachita zadama ndi mtsikana wa zaka 16 za kubadwa.

Malingana ndi m’neneri wa polisiyi, a Cosmas Kagulo, a Mapoko anapalana ubwenzi wa mseli ndi mtsikanayu ndipo abale ake ndi amene anakawaneneza ku polisi atawaona akutulukira m’munda wina kumeneko.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Akubanja la Chilima ayamika boma ndi a Malawi

Mayeso Chikhadzula

CSOs launch Election Integrity Forum

Eunice Ndhlovu

Apolisi amanga mlonda pomuganizira kuti anaba

Davie Umar
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.