Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani

‘Ofesi ya khonsolo ya Mangochi yatsopano idzathandiza koposa’

Ntchito yomanga ofesi ya tsopano ya khonsolo ya Mangochi akuti ithandiza kwambiri m’mene adindo amagwilira ntchito.

Izi zili chomwechi kaamba koti adindo anthambi zambiri zofunikira adzigwira ntchito pamalo amodzi kusiyana ndi mmene zinthu zilili pano pamene ofesi zili mbali ina ya town ya Mangochi.

Mtsogoleri wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, masanawa anayendera ntchito yomanga ofesiyi ndipo anabzyalapo mtengo.

Pakadali pano, Dr Chakwera ndi Mayi Monica Chakwera anyamuka ulendo opita kukayendera ntchito yomanga msewu wa Monkey Bay – Cape Maclear.

Olemba: Owen Mavula

Related posts

Oxfam adds voice to call for aid for countries hit by hunger and flooding crisis

Rabson Kondowe

SDA Church equips youths with social skills

McDonald Chiwayula

Christ Alive Family Church marks 20 years of service

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.