Malawi Broadcasting Corporation
Agriculture Business Development Local Local Nkhani

Admarc idzigula chimanga pamtengo okwera

Bungwe la Admarc tsopano lidzigula chimanga pa mtengo wa K700 pa kilogramme (K35,000 pa thumba la 50 kilogrammes), malinga ndi mkulu wa bungweli, a Daniel Makata.

Mtengowu wakwera kuchoka pa K650 pa kilogramme (K32,500 pa thumba lolemera 50 kilogrammes) umene boma linakhazikitsa ngati poyambira.

A Makata ati Admarc yachita izi pofuna kuwonetsetsa kuti alimi akupindula ndi ulimi monga boma likufunira.

 

Related posts

Government addressing challenges — Chihana

Rabson Kondowe

Lands Ministry asked to fast track construction of houses for people with albinism

Romeo Umali

Inclusive social protection crucial for persons with disabilities

Blessings Kanache
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.