Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Usi ali ku mapemphero

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi akuchita nawo mapemphero pa mpingo wa Zambezi Evangelical ku Mitsidi mu mzinda wa Blantyre.

Pampingopa palinso chikondwerero chokhazikitsa mlembi wamkulu pa mpingowu, m’busa Robert Yanduya.

Dr Usi analandiridwa ndi abusa komanso akuluakulu ampingowu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malawi Olympic Committee calls for more investment

MBC Online

Piksy gears up for new album

Romeo Umali

Flames to face reigning COSAFA champions

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.