Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Tizidziwa zotsatira za kafukufuku — MPUC

Bungwe loona zachitetezo ndi umodzi m’dziko muno la Malawi Peace and Unity Commission (MPUC) lapempha mabungwe komanso adindo kuti adzichita changu pofufuza nkhani komanso kubweretsa zotsatira zake poyera.

Wapampando wa bungwe la MPUC, a Mary Mkosi, ati kuchita motero kuthandiza kuti anthu omwe salemekeza malamulo a dziko la Malawi adzionekera ng’amba komanso adzilangidwa.

A Mkosi anapemphanso a Malawi kuti adzilemekeza mabwalo a milandu maka nthawi yomwe mabwaalowaakupanmga chigamulo.

Iwo amanena izi mu mzinda wa Lilongwe pamsonkhano wa olembankhani omwe cholinga chake unali kuwunikira zina mwandondomeko zabungweli.

 

Related posts

Ntchito za umoyo zipitilira kuyenda bwino — Boma

Romeo Umali

MERA CAUTIONS ON ILLEGAL FUEL VENDING AND HOARDING

MBC Online

Ascent Academy drawn in Group B for CAF Women’s Champions League

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.