Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Oimba aphunzire kugwira ntchito ndi aluso ena — Billy Kaunda

Billy Kaunda walangiza oimba kuti aphunzire kugwira ntchito ndi aluso ena monga alakatuli.
Kaunda wayankhula izi pomwe wati akubwera ndi chimbale chatsopano posachedwapa momwe Okoma Atani Malunga, katswiri pandakatulo, wamulembera nyimbo zingapo.
“Sikoyamba kugwira ntchito ndi a Malunga pankhani yanyimbo, anandipatsapo ndakatulo ya ‘Naliyera’ komanso ‘Mawu Angawa’ mwazina,” anatero Billy Kaunda.
Iye wati pakadalipano akutangwanika ndi ntchito zina monga zakunyumba yamalamulo ngakhale wati zokhudza chimbale chake zilimchimake.
Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malawi diaspora in South Africa honours Mlotchwa family’s 46 years of service

McDonald Chiwayula

Analysts say Mabedi has a big task

Romeo Umali

Unity of purpose critical in combating cyber threats — First Lady

Olive Phiri
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.