Malawi Broadcasting Corporation
Local Local News Nkhani Religion

Dr Usi akhazikitsa nawo Malawi Church and Community Transformation Movement

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino Dr Michael Usi ali nawo pa zochitika zokhazikitsa bungwe la Malawi Church and Community Transformation Movement m’chigawo cha kum’mwera.

Bungweli ndi lopangidwa ndi atsogoleri amipingo ndipo lidzigwira ntchito ndi mafumu komanso anthu osiyanasiyana.

Cholinga chake ndi kulimbikitsa ntchito zabwino m’magawo osiyanasiyana a chitukuko.

Dr Usi anayenda nawo pa ulendo wa ndawala kuchoka ku HHI mpakana pa mpingo wa Word Alive International Ministries munzinda wa Blantyre.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

FCB Nyasa Big Bullets elevate Fodya, others to managerial positions

Romeo Umali

Floodlight semis — Bullets Vs Karonga

MBC Online

NGO steps in to assist hunger-stricken families in Balaka

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.