Malawi Broadcasting Corporation
Local Nkhani

Dekhani AMalawi zikutheka — Chakwera

Prezidenti wa dziko lino, Dr Lazarus Chakwera, watsimikizira anthu a m’boma la Dowa kuti vuto la madzi likhala mbiri ya makedzana.

Poyankhula kwa khwimbi la anthu limene linasonkhana pa Madisi Trading Centre, Dr Chakwera wati kubwera kwa chitukuko cha madzi Cha Kholongo Multipurpose Dam zithandizira kwambiri kusintha miyoyo ya anthu a m’boma la Dowa ndi madela wozungulira.

Pa chifukwachi, mtsogoleri wa dziko linoyu wapempha aMalawi kuti adekhe pomwe akukhazikitsa zitukuko zosiyanasiyana mokomera aMalawi onse.

Chitukuko cha madzi cha Kholongo Multipurpose Dam chikuyembekeza kutha chaka cha mawa.

Related posts

Nkhani sindalama koma zomwe Bullets yachita – Silver Strikers

Alinafe Mlamba

23-year-old man gets eight years for defilement

Romeo Umali

Likoma residents for expedited jetty completion

Rabson Kondowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.