Malawi Broadcasting Corporation
Local Local Sports Sports

Matimu athamanga — Ramadhan

Mphunzitsi watsopano wa timu ya Mighty Wanderers, Nsanzurwimo Ramadhan, wachenjeza matimu m’dziko muno kuti akonzekere kuchita wefuwefu chifukwa athamanga ngati akufuna afanane ndi ukadaulo wake.

Ramadhan wanena izi pabwalo la ndege la Chileka mumzinda wa Blantyre pofika m’dziko muno kuchokera m’dziko la Tanzania.

Ramadhan anakhalako mphunzitsi wa timu ya dziko lino ya The Flames komanso FCB Nyasa Big Bullets.

Malinga ndi bungwe la FAM,ligi ya masewero a mpira wa miyendo m’dziko muno iyamba mmwezi wa April.

#MBCOnlineServices

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Salima Sugar ikupereka K500 million kwa osamuka m’minda yawo

Foster Maulidi

Loans not gifts, must be repaid- NEEF

MBC Online

Bangwe All Stars faults officiation for draw against Moyale Barracks

Rudovicko Nyirenda
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.