Malawi Broadcasting Corporation
Entertainment Entertainment Local Local Music News Nkhani

Giboh Pearson wapulumuka ku ngozi

Katswiri oyimba amene amachokera m’boma la Phalombe, Giboh Pearson, wapulumuka pa ngozi ya galimoto yomwe wachita pomwe amapita ku phwando la msangulutso ku Bangwe mu mzinda wa Blantyre.

Malinga ndi Pearson, chiwongolero komanso mabuleki agalimoto lake zinasiya kugwira ntchito, zomwe zinachititsa kuti akanike kuwongolera galimotoli ndipo linatembenuzika.

“Ndachita ngozi koma ndili bwino,” watero Giboh patsamba lake la mchezo.

Pangoziyi palibe wavulala.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Voter registration supervisors urged to uphold legal standards

MBC Online

Mwambo wapachaka wa Kungoni Arts and Culture wayamba

Charles Pensulo

Onesmus strikes a chord in SA soapie

Alinafe Mlamba
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.