Malawi Broadcasting Corporation
Crime Local Local News Nkhani

Apolisi amanga mlonda pomuganizira kuti anaba

Apolisi m’boma la Mangochi amanga a Smith White, 32, powaganizira kuti anaba zipangizo zomangira nyumba za K30 million ku Savijan Cottage komwe amagwirako ntchito ngati mlonda.

Ofalitsa nkhani ku Polisi ya Mangochi, a Amina Tepani Daud, ati atachita kafukufuku anapeza kuti a White anagulitsa katunduyi yemwe amangokhala.

A Daudi ati mwini wakeyo atazindikira izi, anakanena ku polisi ndipo apolisiwo anapeza wina mwa katunduyi yemwe ndi wa ndalama zokwana K20 million.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Traders unhappy with multiple roadblocks

Earlene Chimoyo

Silver Strikers eliminates Bullets’ title defence hopes

Romeo Umali

Local authorities urged to lead implementation of physical development plans

Olive Phiri
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.