Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Kampani zamigodi ziyike umwini pa MSE — Misalico

Bungwe la Minority Shareholders Association of Listed Companies (Misalico) lati boma liwonetsetse kuti kampani za migodi zidziyika umwini wake wina pa msika wa Malawi Stock Exchange (MSE) kuti a Malawi adzigula nawo magawo.

Mlembi wa bungweli, a Frank Harawa, amafotokoza izi pamene msonkhano wa zamigodi watha lero mu mzinda wa Lilongwe.

Bungwe la Misalico ndi la anthu amene ali ndi masheya pa msika wa Malawi Stock Exchange.

Mukanema ali m’munsiyu, a Harawa akufotokoza zambiri.

Related posts

NASFAM for youth involvement in agriculture

Romeo Umali

Malawi, Botswana strengthen ties

Rabson Kondowe

Human Trafficking persists

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.