Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News Nkhani

Msonkho pa ma belo wabwerera kuzakale

Mkulu wabungwe lotolera misonkho, a John Biziwick, walamula kuti ogwira ntchito kubungweli aleke kugwiritsa ntchito msonkho okwera pa mabelo a zovala, umene anaukhazikitsa posachedwapa.

Izi zikudza patangodutsa nthawi yochepa ochita malonda amtunduwu munzinda wa Lilongwe atachita zionetsero ndikukapereka madandaulo awo ku ofesi za bungweli.

Related posts

Chomanika calls for accelerated action in fighting climate change

Rabson Kondowe

Dallas ready to host US-Summit

Rabson Kondowe

MoH, MRCS urge legislators to earmark local funds for WASH

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.