Malawi Broadcasting Corporation
News

Mlandu wa a Bushiri ukupitilira lero

Mneneri Shepherd Bushiri ndi mkazi wake Mary lero ali kubwalo lamilandu la Resident Magistrate ku Lilongwe.

Bwalo lamilanduli likumva pempho la boma la South Africa kuti a Bushiri akayankhire milandu yawo m’dzikolo.

Oimira a Bushiri ndi akazi awo pamlanduwu lero akuyenera kupitilira kufunsa mboni yaboma yochokera m’dziko la South Africa, a Sibongire Mnzinyathi, omwenso ndi ozenga milandu ku Gauteng m’dzikolo, pa zomwe akudziwa pamlanduwu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Katanda to launch book on mental health

Romeo Umali

NCST encourages journalists to champion biotech

MBC Online

Right to food project transforming lives in Mangochi

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.