Malawi Broadcasting Corporation
Culture Local News Nkhani Politics

‘Enock Chihana apepese’

Bungwe la Chewa Heritage Malawi – Chifukwato cha a Chewa lauza a Enock Chihana kuti apepese mtundu wa a Chewa pazimene adayankhula pamsonkhano wa olembankhani Lachitatu munzinda wa Lilongwe.

Iwo ati a Chihana adayankhula mawu achipongwe pa msonkhanowo.

Wapampando wa bungweli, Mfumu Sosola, ati bungwe lawo lapereka masiku atatu kwa a Chihana kuti apepese kupanda kutero adzawaitana kuti akawaonetse kudambwe.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Government, MAGGA urge youths to combat drug and alcohol abuse

MBC Online

PRISAM lauds Chakwera’s move to increase student allowances

Rabson Kondowe

Dr Chakwera adzudzula mchitidwe wa chidodo pa ntchito

MBC Online
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.