Minister of Information Moses Kunkuyu says a team of experts from Germany will arrive in the country this Saturday to investigate the plane crash that...
Wapampando watsopano wa bungwe loyendetsa zisankho la MEC, Justice Annabel Mtalimanja, alumbilitsidwa lachisanu pa 21 June, 2024 ku Lilongwe High court nthawi ya 9 koloko...
Katswiri pa utsogoleri ndi ufulu wa anthu, a Undule Mwakasungula, ati kusankhidwa kwa Justice Annabel Mtalimanja ngati wapampando wa bungwe la MEC ndi chilimbikitso kwa...
Apolisi ku Lilongwe agwira anthu awiri omwe akuwaganizira kuti akukhudzidwa ndi kubedwa kwa katundu wambiri mu mzindawu komanso kuchita ziwembu. M’neneri wa Polisi ya Kanengo,...
Anthu asanu ndi atatu amene amakumba manda ku manda a Area 18, pansi pa Lilongwe City Council, alandira njinga komanso K250,000 aliyense ngati njira imodzi...
The Malawi National Football Team have maintained their 125th position in the latest FIFA rankings. According to the rankings released today by FIFA, the Flames’...
Chitipa United have appointed Christopher Nyambose as their head coach on a one-year contract, replacing McNelbert Kazuwa who resigned last month. Nyambose re-joins Chitipa after...
Mkulu wa bungwe lowulutsa mawu la Malawi Broadcasting Corporation (MBC), a George Kasakula, ati bungwe lawo lidzagwira ntchito mwaukadaulo ndi mopanda kukondera pa chisankho cha...
Anthu okhala mu nzinda wa Lilongwe omwe analembetsa mu ndondomeko ya Mtukula Pakhomo wam’mizinda akuyembekezeka kulandira ndalamazi lachinayi, zomwe ndi K150,000 aliyense. Anthu 22 339...