22
August

22/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3112 times

Mkazi agenda mwamuna wake ndi mwala

Mwamuna wina kwa Mayaka mboma la Zomba ali pa ululu woopsya kwambili mkazi wake atamuvulaza pomugenda ndi mwala ku nkhongo.

18
August

18/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 3314 times

Mwambo wamapemphero usokonekela
Mwambo wamapemphero a chitsitsimutso wasokonezeka ku Nchalo m’boma la Chikwawa.

17
August

17/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 5183 times

Asiidwa banja kamba kosakhulupilika

Mkulu wina mboma la Salima manja ali ku nkhongo mwamuna wake atamusasa kuti sakumufunanso banja kamba kosakhulupirika.

16
August

16/08/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4232 times

Chidakwa chisekesa anthu

Chidakwa china mdera la Makwangwala m’boma la Ntcheu chinaseketsa anthu. Nkhaniyi ikuti mwamunayo anakwatila zaka zitatu zapitazo ndipo wakhala ali pa chikamwini mderalo.

Get Your Newsletter