30
June

30/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4272 times

Apasidwa makofi kamba kodyesa anthu nyama ya fisi
Mnyamata wina kwa Nkalo mboma la Chiradzulu amutuwisa ndi zibakera chifukwa chowadyesa anthu am’deralo nyama ya fisi powanamiza kuti ndi ya Ng’ombe.

28
June

28/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 5079 times

Dalaivala akunthidwa atagwidwa akuchita zadama
Dalaivala wina ku Blantyre amukuntha kodetsa nkhawa mdela la Kwacha atamupezelela akuchita zachisembwere ndi mai wina mgalimoto lake.

24
June

24/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 6303 times

Asekedwa kamba ka nkhuli
Mwamuna wina akumuseka kwa Sub-T.A. Ngwelero m’boma la Zomba kamba ka nkhuli yomwe ali nao.

20
June

20/06/17

Written by
Published in Nkhani Zam'maboma
Read 4055 times

M'busa agwidwa akusamba usiku panja
Mbusa wampingo wina kwa Mgona A ku Kanengo mu mzinda wa Lilongwe akuyenda mogwetsa nkhope yake pansi chifukwa cha manyazi atamutulukila kuti amasamba usiku uli onse 10 –kokolo kwinaku akuzungulila nyumba.

Get Your Newsletter