Mwamuna wina ku Migowi m’boma la Phalombe yemwe anali pa ubwenzi wa ntseri ndi mkazi wamwini wachimina.
Ntchembere zina ku Fatima m’dera la mfumu Mlolo m’boma la Nsanje zinakalipira mai wina wa mwana m’modzi poyankhula zoduka mutu pagulu.
Mai wina ku Blantyre akuyenda mogwetsa nkhope yake pansi chifukwa cha manyazi.
Mtengwa wina mdera la Kacheche ku Mzimba ati sakumvetsa ndi zomwe zamuchitikira.