Malawi Broadcasting Corporation
News

Mlandu wa a Bushiri ukupitilira lero

Mneneri Shepherd Bushiri ndi mkazi wake Mary lero ali kubwalo lamilandu la Resident Magistrate ku Lilongwe.

Bwalo lamilanduli likumva pempho la boma la South Africa kuti a Bushiri akayankhire milandu yawo m’dzikolo.

Oimira a Bushiri ndi akazi awo pamlanduwu lero akuyenera kupitilira kufunsa mboni yaboma yochokera m’dziko la South Africa, a Sibongire Mnzinyathi, omwenso ndi ozenga milandu ku Gauteng m’dzikolo, pa zomwe akudziwa pamlanduwu.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Mwaungulu, Gumbo win Goal of the Month award

MBC Online

A ‘hand of hope’ for orphans

MBC Online

Launch of Tambala Cup this weekend

Timothy Kateta
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.