Malawi Broadcasting Corporation
News

Mlandu wa a Bushiri ukupitilira lero

Mneneri Shepherd Bushiri ndi mkazi wake Mary lero ali kubwalo lamilandu la Resident Magistrate ku Lilongwe.

Bwalo lamilanduli likumva pempho la boma la South Africa kuti a Bushiri akayankhire milandu yawo m’dzikolo.

Oimira a Bushiri ndi akazi awo pamlanduwu lero akuyenera kupitilira kufunsa mboni yaboma yochokera m’dziko la South Africa, a Sibongire Mnzinyathi, omwenso ndi ozenga milandu ku Gauteng m’dzikolo, pa zomwe akudziwa pamlanduwu.

Related posts

Journalists drilled on New Pension Law

Romeo Umali

Women’s voices spur better health service delivery in Chiradzulu

Rabson Kondowe

Govt committed to bolster ICT

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.