Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Mbali ina ya msewu wa Chiwembe sanamange bwino — Chimwendo Banda

Nduna yoona za maboma aang’ono komanso umodzi ndi chikhalidwe, a Richard Chimwendo Banda, yati siyokhutitsidwa ndi m’mene gawo lina la msewu wa Chiwembe mu mzinda wa Blantyre awumangira.

Iyo imanena izi itayendera misewu yamadulira imene akuimanga mu mzindawu, ndipo iwo ati nkhaniyi asiyira akuluakulu oona za mamangidwewa.

Komabe, a Chimwendo Banda ati ndi okondwa kuti miseu yambiri yamangidwa bwino.

Olemba : Blessings Cheleuka

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

FISCAL POLICE NAB MULLI, MUHARA

MBC Online

NPC re-emphasises youth inclusion for MW2063 realisation

MBC Online

Govt for people-centred ecosystem conservation

Kenneth Jali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.