Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Kampani zamigodi ziyike umwini pa MSE — Misalico

Bungwe la Minority Shareholders Association of Listed Companies (Misalico) lati boma liwonetsetse kuti kampani za migodi zidziyika umwini wake wina pa msika wa Malawi Stock Exchange (MSE) kuti a Malawi adzigula nawo magawo.

Mlembi wa bungweli, a Frank Harawa, amafotokoza izi pamene msonkhano wa zamigodi watha lero mu mzinda wa Lilongwe.

Bungwe la Misalico ndi la anthu amene ali ndi masheya pa msika wa Malawi Stock Exchange.

Mukanema ali m’munsiyu, a Harawa akufotokoza zambiri.

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Awamanga ataba matumba 300 a chimanga cha ADMARC

Charles Pensulo

Nzika yaku Mozambique ayigwira itathyola ndikuba mnyumba

Charles Pensulo

Centenary Bank to construct cancer facility at Likuni Hospital

Yamikani Simutowe
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.