Malawi Broadcasting Corporation
Business Development Local Local News

Kampani zamigodi ziyike umwini pa MSE — Misalico

Bungwe la Minority Shareholders Association of Listed Companies (Misalico) lati boma liwonetsetse kuti kampani za migodi zidziyika umwini wake wina pa msika wa Malawi Stock Exchange (MSE) kuti a Malawi adzigula nawo magawo.

Mlembi wa bungweli, a Frank Harawa, amafotokoza izi pamene msonkhano wa zamigodi watha lero mu mzinda wa Lilongwe.

Bungwe la Misalico ndi la anthu amene ali ndi masheya pa msika wa Malawi Stock Exchange.

Mukanema ali m’munsiyu, a Harawa akufotokoza zambiri.

Related posts

Mega farm initiative transforms life of a pensioner

Rabson Kondowe

Osagwiritsa ntchito imfa ya Chilima pa ndale

Rabson Kondowe

Morocco to host 9th Ministerial Meeting with Gulf Cooperation Council

McDonald Chiwayula
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.