Mikoko yogona komanso anthu wothandiza pa ntchito zachitetezo pa mudzi wa Mambo kwa Jenala m’boma la Phalombe akufuna-funa amuna ena anai omwe avulala mlimi wina wa nzimbe.
Mikoko yogona komanso anthu wothandiza pa ntchito zachitetezo pa mudzi wa Mambo kwa Jenala m’boma la Phalombe akufuna-funa amuna ena anai omwe avulala mlimi wina wa nzimbe.
Anthu a m’mudzi wina mdera la mfumu Tambala m’boma la Dedza akukhalira kuseka mai wina yemwe anabaya mwamuna wake ndi CHIUZIRA - kapena kunena kuti chitsulo chomwe amabowolera mpini wa khasu chifukwa choledzera.
Anthu a m’mudzi wina ku Dwangwa m’boma la Nkhotakota akhumudwa ndi zomwe yachita njonda ina yapa banja polola mzake kukasangalala ndi chibwenzi chake mnyumba mwake mkazi wake atapita ku msika.