Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News

Tizidziwa zotsatira za kafukufuku — MPUC

Bungwe loona zachitetezo ndi umodzi m’dziko muno la Malawi Peace and Unity Commission (MPUC) lapempha mabungwe komanso adindo kuti adzichita changu pofufuza nkhani komanso kubweretsa zotsatira zake poyera.

Wapampando wa bungwe la MPUC, a Mary Mkosi, ati kuchita motero kuthandiza kuti anthu omwe salemekeza malamulo a dziko la Malawi adzionekera ng’amba komanso adzilangidwa.

A Mkosi anapemphanso a Malawi kuti adzilemekeza mabwalo a milandu maka nthawi yomwe mabwaalowaakupanmga chigamulo.

Iwo amanena izi mu mzinda wa Lilongwe pamsonkhano wa olembankhani omwe cholinga chake unali kuwunikira zina mwandondomeko zabungweli.

 

Print Friendly, PDF & Email

Related posts

Malawi-Mozambique project operational by September

Charles Pensulo

Kwacha holds firm against US Dollar

MBC Online

Social Media misinformation worries government

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.