Malawi Broadcasting Corporation
Development Local Local News Nkhani

Tikuyesetsa kuti magetsi ayake mwachangu, ESCOM yatero

Bungwe la ESCOM lati makina ake a magetsi anadzithimitsa lero nthawi itatsala mphindi 18 kuti ikwane 12 koloko masana.

Malinga ndi chikalata chomwe a ESCOM atulutsa, pakadali pano iwo akuyesetsa kubwezeretsa magetsi m’madera ambiri ngakhale m’madera ena magetsi sanayakebe.

Iwo ati pomwe akufufuza kuti apeze chomwe chinachititsa kuti magetsi azime, akuyesetsanso kubwezeretsa komwe sanayambe kuyaka.

 

Related posts

Duo arrested for betting shop theft

Alinafe Mlamba

Government re-commits to digitalise education in Malawi

Romeo Umali

Govt praises activist late Chiwaula

Romeo Umali
error: All Content is protected. Copyright © 2022. Malawi Broadcasting Corporation. All Right Reserved.